Mika 1:12 - Buku Lopatulika12 Pakuti wokhala mu Maroti alindira chokoma, popeza choipa chatsika kwa Yehova kunka kuchipata cha Yerusalemu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Pakuti wokhala m'Maroti alindira chokoma, popeza choipa chatsika kwa Yehova kunka kuchipata cha Yerusalemu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Anthu a ku Maroti ali ndi nkhaŵa poyembekeza thandizo, chifukwa Chauta wadzetsa chiwonongeko pafupi ndi Yerusalemu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Anthu amene amakhala ku Maroti akubuwula ndi ululu, akuyembekezera thandizo, chifukwa Yehova wabweretsa tsoka, lafika mpaka pa chipata cha Yerusalemu. Onani mutuwo |