Mika 1:1 - Buku Lopatulika1 Mau a Yehova amene anadza kwa Mika wa ku Moreseti masiku a Yotamu, Ahazi, ndi Hezekiya, mafumu a Yuda, amene adaona za Samariya ndi Yerusalemu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Mau a Yehova amene anadza kwa Mika wa ku Moreseti masiku a Yotamu, Ahazi, ndi Hezekiya, mafumu a Yuda, amene adaona za Samariya ndi Yerusalemu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Pa nthaŵi ya ufumu wa Yotamu, Ahazi ndi Hezekiya, mafumu a ku Yuda, Chauta adampatsa mthenga Mika wa ku Moreseti. Nazi zimene iyeyu adaona m'masomphenya zokhudza Samariya ndi Yerusalemu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Yehova anayankhula ndi Mika wa ku Moreseti pa nthawi ya ulamuliro wa Yotamu, Ahazi ndi Hezekiya, mafumu a ku Yuda. Awa ndi masomphenya amene iye anaona onena za Samariya ndi Yerusalemu. Onani mutuwo |