Mika 1:2 - Buku Lopatulika2 Imvani, mitundu ya anthu, inu nonse; tamvera, dziko lapansi, ndi zonse zili m'mwemo; ndipo Ambuye Yehova akhale mboni yakutsutsa inu, Ambuye mu Kachisi wake wopatulika. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Imvani, mitundu ya anthu, inu nonse; tamvera, dziko lapansi, ndi zonse zili m'mwemo; ndipo Ambuye Yehova akhale mboni yakutsutsa inu, Ambuye m'Kachisi wake wopatulika. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Imvani nonsenu anthu a mitundu yonse. Tchera khutu iwe dziko lapansi ndi zonse zokhala m'menemo. Ambuye Chauta akuimbani mlandu, akulankhulira ku Nyumba yao yoyera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Tamverani, inu anthu a mitundu yonse, mvetsera iwe dziko lapansi ndi okhala mʼmenemo, pakuti Ambuye Yehova achitira umboni wokutsutsani, Ambuye akuyankhula ali mʼnyumba yake yopatulika. Onani mutuwo |