Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 9:38 - Buku Lopatulika

38 Chifukwa chake pempherani Mwini zotuta kuti akokose antchito kukututa kwake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

38 Chifukwa chake pempherani Mwini zotuta kuti akokose antchito kukututa kwake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

38 Nchifukwa chake mupemphe Mwini dzinthu kuti atume antchito okatuta dzinthu dzakedzo.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

38 Nʼchifukwa chake, pemphani Ambuye mwini zokolola kuti atumize antchito ku munda wake.”

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 9:38
15 Mawu Ofanana  

Ambuye anapatsa mau, akazi akulalikira uthengawo ndiwo khamu lalikulu.


Munakwera kunka kumwamba, munapita nao undende kuuyesa ndende; munalandira zaufulu mwa anthu, ngakhale mwa opikisana nanu, kuti Yehova Mulungu akakhale nao.


ndipo ndidzakupatsani inu abusa monga mwa mtima wanga, adzakudyetsani inu nzeru ndi luntha.


Ndipo otsala a Yakobo adzakhala pakati pa mitundu yambiri ya anthu, ngati mame ochokera kwa Yehova ngati mvula paudzu, yosachedwera munthu, yosalindira ana a anthu.


Pomwepo ananena kwa ophunzira ake, Zotuta zichulukadi koma antchito ali owerengeka.


Chifukwa chake Yesu anatinso kwa iwo, Mtendere ukhale ndi inu; monga Atate wandituma Ine, Inenso ndituma inu.


Kodi simunena inu, kuti, Yatsala miyezi inai, ndipo kudza kumweta? Onani ndinena kwa inu, Kwezani maso anu, nimuyang'ane m'minda, kuti mwayera kale kufikira kumweta.


Ndipo pa kutumikira Ambuye iwowa, ndi kusala chakudya, Mzimu Woyera anati, Mundipatulire Ine Barnabasi ndi Saulo ku ntchito imene ndinawaitanirako.


Pamenepo ndipo iwo akubalalitsidwa anapitapita nalalikira mauwo.


Ndipotu Mulungu anaika ena mu Mpingo, poyamba atumwi, achiwiri aneneri, achitatu aphunzitsi, pamenepo zozizwa, pomwepo mphatso za machiritso, mathandizo, maweruziro, malilime a mitundumitundu.


Ndipo Iye anapatsa ena akhale atumwi; ndi ena aneneri; ndi ena alaliki; ndi ena abusa, ndi ena aphunzitsi;


Chotsalira, abale, mutipempherere, kuti mau a Ambuye athamange, nalemekezedwe, monganso kwanu;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa