Mateyu 9:38 - Buku Lopatulika38 Chifukwa chake pempherani Mwini zotuta kuti akokose antchito kukututa kwake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201438 Chifukwa chake pempherani Mwini zotuta kuti akokose antchito kukututa kwake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa38 Nchifukwa chake mupemphe Mwini dzinthu kuti atume antchito okatuta dzinthu dzakedzo.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero38 Nʼchifukwa chake, pemphani Ambuye mwini zokolola kuti atumize antchito ku munda wake.” Onani mutuwo |