Mateyu 9:37 - Buku Lopatulika37 Pomwepo ananena kwa ophunzira ake, Zotuta zichulukadi koma antchito ali owerengeka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201437 Pomwepo ananena kwa ophunzira ake, Zotuta zichulukadi koma antchito ali owerengeka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa37 Tsono adauza ophunzira ake kuti, “Dzinthu ndzochulukadi, achepa ndi antchito. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero37 Pamenepo anati kwa ophunzira ake, “Zokolola ndi zambiri koma antchito ndi ochepa. Onani mutuwo |