Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 9:26 - Buku Lopatulika

26 Ndipo mbiri yake imene inabuka m'dziko lonse limenelo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

26 Ndipo mbiri yake imene inabuka m'dziko lonse limenelo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

26 Mbiri imeneyi idawanda m'dera lonselo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

26 Mbiriyi inamveka mʼdera lonse.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 9:26
11 Mawu Ofanana  

Ndipo mbiri yake inabuka ku Siriya konse: ndipo anatengera kwa Iye onse akudwala, ogwidwa ndi nthenda ndi mazunzo a mitundumitundu, ndi ogwidwa ndi ziwanda, ndi akhunyu, ndi amanjenje; ndipo Iye anawachiritsa.


Koma iwo anatulukamo, nabukitsa mbiri yake m'dziko lonselo.


Ndipo mbiri yake inabuka pompaja kudziko lonse la Galileya lozungulirapo.


Koma iye anatuluka nayamba kulalikira ndithu, ndi kubukitsa mauwo, kotero kuti Yesu sanathe kulowanso poyera m'mudzi, koma anakhala padera m'mapululu; ndipo anadza kwa Iye anthu a kumalo onse.


Ndipo mfumu Herode anamva izi; pakuti dzina lake lidamveka; ndipo ananena, kuti, Yohane Mbatizi wauka kwa akufa, ndipo chifukwa chake mphamvu izi zichitachita mwa Iye.


Ndipo Yesu anabwera ndi mphamvu ya Mzimu ku Galileya; ndipo mbiri yake ya Iye inabuka ku dziko lonse loyandikira.


Ndipo mbiri yake ya Iye inafalikira kumalo onse a dziko loyandikira.


Koma makamaka mbiri yake ya Iye inabuka: ndipo mipingo yambiri ya anthu inasonkhana kudzamvera, ndi kudzachiritsidwa nthenda zao.


Ndipo mbiri yake imeneyo inabuka ku Yudeya yense, ndi ku dziko lonse loyandikira.


Pakuti mfumuyo idziwa izi, kwa iye imene ndilankhula nayonso mosaopa: pakuti ndidziwadi kuti kulibe kanthu ka izi kadambisikira; pakuti ichi sichinachitike m'tseri.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa