Mateyu 9:25 - Buku Lopatulika25 Koma pamene khamulo linatulutsidwa, Iye analowamo, nagwira dzanja lake; ndipo kabuthuko kadauka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Koma pamene khamulo linatulutsidwa, Iye analowamo, nagwira dzanja lake; ndipo kabuthuko kadauka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Koma onsewo atatulutsidwa, Yesu adaloŵa, nagwira mtsikanayo pa dzanja, iye nkuuka. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Atangowatulutsa anthuwo, analowa mʼnyumba ndipo anagwira dzanja la mtsikanayo ndipo anauka. Onani mutuwo |