Mateyu 9:24 - Buku Lopatulika24 ananena, Tulukani, pakuti kabuthuko sikanafe koma kali m'tulo. Ndipo anamseka Iye pwepwete. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 ananena, Tulukani, pakuti kabuthuko sikanafa koma kali m'tulo. Ndipo anamseka Iye pwepwete. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Tsono Iye adaŵauza kuti, “Tatulukani! Mtsikanayutu sadamwalire ai, ali m'tulo chabe.” Pamenepo anthuwo adayamba kumseka monyodola. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 anati, “Tulukani, mtsikanayu sanafe koma ali mtulo.” Koma anamuseka Iye. Onani mutuwo |