Mateyu 9:23 - Buku Lopatulika23 Ndipo Yesu polowa m'nyumba yake ya mkuluyo, ndi poona oimba zitoliro ndi khamu la anthu obuma, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Ndipo Yesu polowa m'nyumba yake ya mkuluyo, ndi poona oimba zitoliro ndi khamu la anthu obuma, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Pamene Yesu adafika kunyumba kwa mkulu uja, adaona anthu oimba zitoliro, ndiponso anthu ambiri obuma. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Yesu atalowa mʼnyumba ya mkulu wa sunagoge ndi kuona oyimba zitoliro ndi gulu la anthu ochita phokoso, Onani mutuwo |