Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 8:7 - Buku Lopatulika

7 Ndipo Yesu ananena naye, Ndifika Ine, ndidzamchiritsa iye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Ndipo Yesu ananena naye, Ndifika Ine, ndidzamchiritsa iye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Yesu adamuuza kuti, “Chabwino, ndibwera kudzamchiritsa.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Ndipo Yesu anati kwa iye, “Ine ndibwera kudzamuchiritsa.”

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 8:7
5 Mawu Ofanana  

nati, Ambuye, mnyamata wanga ali gone m'nyumba wodwala manjenje, wozunzidwa koopsa.


Koma kenturiyoyo anavomera nati, Ambuye, sindiyenera kuti mukalowe pansi pa tsindwi langa iai; koma mungonena mau, ndipo adzachiritsidwa mnyamata wanga.


Ndipo Yesu anapita nao. Ndipo pakufika Iye tsono pafupi pa nyumba yake, kenturiyo anatuma kwa Iye abwenzi ake, kunena naye, Ambuye, musadzivute; pakuti sindiyenera ine kuti mudzalowe pansi pa tsindwi langa;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa