Mateyu 8:6 - Buku Lopatulika6 nati, Ambuye, mnyamata wanga ali gone m'nyumba wodwala manjenje, wozunzidwa koopsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 nati, Ambuye, mnyamata wanga ali gone m'nyumba wodwala manjenje, wozunzidwa koopsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Adampempha kuti, “Ambuye, wantchito wanga ali gone kunyumbaku. Sakutha kuyenda, ndipo akumva kupweteka kwambiri.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 nati, “Ambuye, wantchito wanga ali chigonere ku nyumba, sakuthanso kuyenda, akumva kuwawa kwambiri.” Onani mutuwo |