Mateyu 8:22 - Buku Lopatulika22 Koma Yesu ananena kwa iye, Tsata Ine, nuleke akufa aike akufa ao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Koma Yesu ananena kwa iye, Tsata Ine, nuleke akufa aike akufa ao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Koma Yesu adamuuza kuti, “Iweyo unditsate, aleke akufa aziika akufa anzao.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Koma Yesu anamuwuza kuti, “Nditsate Ine ndipo uwaleke akufa ayikane akufa okhaokha.” Onani mutuwo |