Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 8:21 - Buku Lopatulika

21 Ndipo wina wa ophunzira ake anati kwa Iye, Ambuye, mundilole ine ndiyambe ndamuka kuika maliro a atate wanga.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

21 Ndipo wina wa ophunzira ake anati kwa Iye, Ambuye, mundilole ine nditange ndamuka kuika maliro a atate wanga.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

21 Wophunzira wake wina adauza Yesu kuti, “Ambuye, mundilole ndiyambe ndakaika maliro a atate anga.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

21 Wophunzira wina anati kwa Iye, “Ambuye, mundilole ndiyambe ndakayika maliro a abambo anga.”

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 8:21
10 Mawu Ofanana  

Atero Yehova wa makamu, akuti, Anthu awa anena, Nthawi siinafike, nthawi yakumanga nyumba ya Yehova.


Ndipo onse amene adasiya nyumba, kapena abale, kapena alongo, kapena atate, kapena amai, kapena ana, kapena minda, chifukwa cha dzina langa, adzalandira zobwezeredwa zambirimbiri, nadzalowa moyo wosatha.


Ndipo Yesu ananena kwa iye, Ankhandwe ali nazo nkhwimba zao, ndi mbalame za m'mlengalenga zisa zao, koma Mwana wa Munthu alibe potsamira mutu wake.


Koma Yesu ananena kwa iye, Tsata Ine, nuleke akufa aike akufa ao.


Kotero kuti ife sitidziwanso munthu tsopano monga mwa thupi; ndipo ngati tazindikira Khristu monga mwa thupi, koma tsopano sitimzindikiranso motero.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa