Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 8:23 - Buku Lopatulika

23 Ndipo pamene Iye atalowa m'ngalawa, ophunzira ake anamtsata Iye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 Ndipo pamene Iye atalowa m'ngalawa, ophunzira ake anamtsata Iye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 Yesu adaloŵa m'chombo, ndipo ophunzira ake adatsagana naye.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 Iye atalowa mʼbwato, ophunzira ake anamutsatira.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 8:23
6 Mawu Ofanana  

Ndipo onani, panauka namondwe wamkulu panyanja, kotero kuti ngalawa inafundidwa ndi mafunde: koma Iye anali m'tulo.


Ndipo Iye analowa m'ngalawa, naoloka, nadza kumzinda kwao.


Ndipo dzuwa lomwelo, pofika madzulo, ananena kwa iwo, Tiolokere tsidya lina.


Ndipo anayankha, nati kwa iwo, Mukani, muuze Yohane zimene mwaziona, nimwazimva; anthu akhungu alandira kuona kwao, opunduka miyendo ayenda, akhate akonzedwa, ogontha akumva, akufa aukitsidwa, kwa aumphawi ulalikidwa Uthenga Wabwino.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa