Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 7:9 - Buku Lopatulika

9 Kapena munthu ndani wa inu, amene pompempha mwana wake mkate, adzampatsa mwala?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Kapena munthu ndani wa inu, amene pompempha mwana wake mkate, adzampatsa mwala?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Ndani mwa inu, mwana wake atampempha buledi, iye nkumupatsa mwala?

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 “Ndani mwa inu, mwana wake akamupempha buledi amamupatsa mwala?

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 7:9
3 Mawu Ofanana  

Kapena pompempha nsomba, adzampatsa iye njoka kodi?


pakuti yense wakupempha alandira; ndi wakufunayo apeza; ndi kwa wogogodayo chitsegulidwa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa