Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 7:10 - Buku Lopatulika

10 Kapena pompempha nsomba, adzampatsa iye njoka kodi?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Kapena pompempha nsomba, adzampatsa iye njoka kodi?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Kapena atampempha nsomba, iye nkumupatsa njoka?

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Kapena ngati mwana apempha nsomba, kodi amamupatsa njoka?

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 7:10
4 Mawu Ofanana  

Chomwecho, ngati inu, muli oipa, mudziwa kupatsa ana anu mphatso zabwino, kopambana kotani nanga Atate wanu wa Kumwamba adzapatsa zinthu zabwino kwa iwo akumpempha Iye?


Kapena munthu ndani wa inu, amene pompempha mwana wake mkate, adzampatsa mwala?


Ndipo monga Mose anakweza njoka m'chipululu, chotero Mwana wa Munthu ayenera kukwezedwa;


Koma ndiopa, kuti pena, monga njoka inanyenga Heva ndi kuchenjerera kwake, maganizo anu angaipsidwe kusiyana nako kuona mtima ndi kuyera mtima zili kwa Khristu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa