Mateyu 7:8 - Buku Lopatulika8 pakuti yense wakupempha alandira; ndi wakufunayo apeza; ndi kwa wogogodayo chitsegulidwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 pakuti yense wakupempha alandira; ndi wakufunayo apeza; ndi kwa wogogodayo chitsegulidwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Paja munthu amene amapempha, ndiye amalandira; amene amafunafuna, ndiye amapeza; ndipo amene amagogoda, ndiye amamtsekulira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Pakuti wopempha aliyense amalandira; ndi wofuna amapeza; ndipo iye amene agogoda, adzamutsekulira. Onani mutuwo |