Mateyu 7:7 - Buku Lopatulika7 Pemphani, ndipo chidzapatsidwa kwa inu; funani, ndipo mudzapeza; gogodani, ndipo chidzatsegulidwa kwa inu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Pemphani, ndipo chidzapatsidwa kwa inu; funani, ndipo mudzapeza; gogodani, ndipo chidzatsegulidwa kwa inu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 “Pemphani ndipo adzakupatsani. Funafunani ndipo mudzapeza, gogodani, ndipo adzakutsekulirani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 “Pemphani ndipo mudzapatsidwa; funafunani ndipo mudzapeza; gogodani ndipo adzakutsekulirani. Onani mutuwo |