Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 7:18 - Buku Lopatulika

18 Sungathe mtengo wabwino kupatsa zipatso zoipa, kapena mtengo wamphuchi kupatsa zipatso zokoma.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Sungathe mtengo wabwino kupatsa zipatso zoipa, kapena mtengo wamphuchi kupatsa zipatso zokoma.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Mtengo wabwino sungabale zipatso zoipa, kapena mtengo woipa kubala zipatso zabwino ai.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Mtengo wabwino sungabale chipatso choyipa, ndi mtengo woyipa sungabale chipatso chabwino.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 7:18
5 Mawu Ofanana  

Chomwecho mtengo wabwino uliwonse upatsa zipatso zokoma; koma mtengo wamphuchi upatsa zipatso zoipa.


Mtengo uliwonse wosapatsa chipatso chokoma, audula, nautaya kumoto.


Pakuti palibe mtengo wabwino wakupatsa zipatso zovunda; kapenanso mtengo woipa wakupatsa zipatso zabwino.


Pakuti thupi lilakalaka potsutsana naye Mzimu, ndi Mzimu potsutsana nalo thupi; pakuti izi sizilingana; kuti zimene muzifuna musazichite.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa