Mateyu 7:17 - Buku Lopatulika17 Chomwecho mtengo wabwino uliwonse upatsa zipatso zokoma; koma mtengo wamphuchi upatsa zipatso zoipa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Chomwecho mtengo wabwino uliwonse upatsa zipatso zokoma; koma mtengo wamphuchi upatsa zipatso zoipa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Chonchonso mtengo uliwonse wabwino umabala zipatso zabwino, koma mtengo woipa umabala zipatso zoipa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Chimodzimodzinso mtengo wabwino umabala chipatso chabwino, koma mtengo woyipa umabala chipatso choyipa. Onani mutuwo |