Mateyu 6:28 - Buku Lopatulika28 Ndipo muderanji nkhawa ndi chovala? Tapenyetsani maluwa akuthengo, makulidwe ao; sagwiritsa ntchito, kapena sapota: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201428 Ndipo muderanji nkhawa ndi chovala? Tapenyetsani maluwa a kuthengo, makulidwe ao; sagwiritsa ntchito, kapena sapota: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa28 “Ndipo mumaderanji nkhaŵa ndi zovala? Onani maluŵa akuthengo m'mene amakulira. Sagwira ntchito kapena kuwomba nsalu ai. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero28 “Ndipo bwanji inu mudera nkhawa za zovala? Onani makulidwe a maluwa akutchire. Sagwira ntchito kapena kuwomba nsalu. Onani mutuwo |