Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 6:29 - Buku Lopatulika

29 koma ndinena kwa inu, kuti angakhale Solomoni mu ulemerero wake wonse sanavale monga limodzi la amenewa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

29 koma ndinena kwa inu, kuti angakhale Solomoni mu ulemerero wake wonse sanavale monga limodzi la amenewa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

29 Komatu kunena zoona, ngakhale mfumu Solomoni yemwe, mu ulemerero wake wonse, sankavala zokongola kulingana ndi limodzi lomwe mwa maluŵa ameneŵa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

29 Ndikukuwuzani kuti angakhale Solomoni mu ulemerero wake sanavale mofanana ndi limodzi la maluwa amenewa.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 6:29
5 Mawu Ofanana  

Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa