Mateyu 6:21 - Buku Lopatulika21 pakuti kumene kuli chuma chako, komwe udzakhala mtima wakonso. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 pakuti kumene kuli chuma chako, komwe udzakhala mtima wakonso. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Pajatu kumene kuli chuma chako, mtima wakonso kokhala nkomweko. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Pakuti kumene kuli chuma chako, mtima wako udzakhala komweko. Onani mutuwo |