Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 6:21 - Buku Lopatulika

21 pakuti kumene kuli chuma chako, komwe udzakhala mtima wakonso.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

21 pakuti kumene kuli chuma chako, komwe udzakhala mtima wakonso.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

21 Pajatu kumene kuli chuma chako, mtima wakonso kokhala nkomweko.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

21 Pakuti kumene kuli chuma chako, mtima wako udzakhala komweko.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 6:21
14 Mawu Ofanana  

Chinjiriza mtima wako koposa zonse uzisunga; pakuti magwero a moyo atulukamo.


Ndipo kudzakhala chilimbiko m'nthawi zako, chipulumutso chambiri, nzeru ndi kudziwa; kuopa kwa Yehova ndiko chuma chake.


Koma maso ako ndi mtima wako sizisamalira kanthu koma kusirira, ndi kukhetsa mwazi wosachimwa, ndi kusautsa, ndi zachiwawa, kuti uzichite.


Iwe Yerusalemu, utsuke mtima wako kuchotsa zoipa kuti upulumuke. Maganizo ako achabe agona mwako masiku angati?


Akubadwa inu a njoka, mungathe bwanji kulankhula zabwino, inu akukhala oipa? Pakuti m'kamwa mungolankhula mwa kusefuka kwake kwa mtima.


Diso ndilo nyali ya thupi; chifukwa chake ngati diso lako lili la kumodzi, thupi lako lonse lidzakhala lowalitsidwa.


Pakuti kumene kuli chuma chanu, komweko kudzakhalanso mtima wanu.


Ulibe gawo kapena cholandira ndi mau awa; pakuti mtima wako suli wolunjika pamaso pa Mulungu.


popeza sitipenyerera zinthu zooneka, koma zinthu zosaoneka; pakuti zinthu zooneka zili za nthawi, koma zinthu zosaoneka zili zosatha.


ine Paulo ndichilemba ndi dzanja langa, ndidzachibwezera ine; kuti ndisanene nawe kuti iwe ndiwe mangawa anga.


Chisomo kwa inu ndi mtendere za kwa Mulungu Atate wathu ndi Ambuye Yesu Khristu.


Tapenyani, abale, kuti kapena ukakhale mwa wina wa inu mtima woipa wosakhulupirira, wakulekana ndi Mulungu wamoyo;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa