Mateyu 6:20 - Buku Lopatulika20 koma mudzikundikire nokha chuma mu Mwamba, pamene njenjete kapena dzimbiri siziononga, ndipo mbala siziboola ndi kuba; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 koma mudzikundikire nokha chuma m'Mwamba, pamene njenjete kapena dzimbiri siziononga, ndipo mbala siziboola ndi kuba; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Koma mudziwunjikire chuma Kumwamba, kumene njenjete kapena dzimbiri siziwononga, ndiponso mbala sizithyola ndi kuba. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Koma mudziwunjikire chuma kumwamba kumene njenjete ndi dzimbiri siziwononga ndipo mbala sizithyola ndi kuba. Onani mutuwo |