Mateyu 6:19 - Buku Lopatulika19 Musadzikundikire nokha chuma padziko lapansi, pamene njenjete ndi dzimbiri ziononga; ndi pamene mbala ziboola ndi kuba: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Musadzikundikire nokha chuma pa dziko lapansi, pamene njenjete ndi dzimbiri ziononga; ndi pamene mbala ziboola ndi kuba: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 “Musadziwunjikire chuma pansi pano, pamene njenjete ndi dzimbiri zimaononga, ndiponso mbala zimathyola ndi kuba. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 “Musadziwunjikire chuma pa dziko lapansi, pamene njenjete ndi dzimbiri zimawononga ndi pamene mbala zimathyola ndi kuba. Onani mutuwo |