Mateyu 6:13 - Buku Lopatulika13 Ndipo musatitengere kokatiyesa, koma mutipulumutse kwa woipayo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ndipo musatitengere kokatiyesa, koma mutipulumutse kwa woipayo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Ndipo musalole kuti tigwe m'zotiyesa, koma mutipulumutse kwa Woipa uja.” [Pakuti ufumu, mphamvu ndi ulemerero ndi zanu kwamuyaya. Amen.] Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Ndipo musatitengere kokatiyesa; koma mutipulumutse kwa woyipayo.’ Onani mutuwo |
kuti adzakuingitsani kukuchotsani kwa anthu, ndi pokhala panu padzakhala pamodzi ndi nyama zakuthengo; ndipo mudzadya udzu ngati ng'ombe, nimudzakhala wokhathamira ndi mame a kumwamba, ndipo zidzakupitirani nthawi zisanu ndi ziwiri, mpaka mudzadziwa kuti Wam'mwambamwamba alamulira mu ufumu wa anthu, naupereka kwa aliyense Iye afuna mwini.