Mateyu 5:47 - Buku Lopatulika47 Ndipo ngati mupatsa moni abale anu okhaokha, muchitanji choposa ena? Kodi angakhale anthu akunja sachita chomwecho? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201447 Ndipo ngati mupatsa moni abale anu okhaokha, muchitanji choposa ena? Kodi angakhale anthu akunja sachita chomwecho? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa47 Ndipo ngati mupatsa moni abale anu okha, mwachitapo chiyani pamenepo choposa ena? Kodi suja ngakhale akunja amachita chimodzimodzi? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero47 Ndipo ngati inu mupatsa moni abale anu okhaokha mukuchita chiyani choposa ena? Kodi ngakhale akunja sachita chimodzimodzi? Onani mutuwo |