Mateyu 5:46 - Buku Lopatulika46 Chifukwa kuti ngati muwakonda akukondana ndi inu mphotho yanji muli nayo? Kodi angakhale amisonkho sachita chomwecho? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201446 Chifukwa kuti ngati muwakonda akukondana ndi inu mphotho yanji muli nayo? Kodi angakhale amisonkho sachita chomwecho? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa46 Ngati mukonda okhawo amene amakukondani, mungalandire mphotho yanji? Kodi suja ngakhale okhometsa msonkho amachita chimodzimodzi? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero46 Ngati mukonda amene akukondani inu, mudzapeza mphotho yanji? Kodi ngakhale amisonkho sachita chimodzimodzi? Onani mutuwo |