Mateyu 5:48 - Buku Lopatulika48 Chifukwa chake inu mukhale angwiro, monga Atate wanu wa Kumwamba ali wangwiro. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201448 Chifukwa chake inu mukhale angwiro, monga Atate wanu wa Kumwamba ali wangwiro. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa48 Nchifukwa chake monga Atate anu akumwamba ali abwino kotheratu, inunso mukhale abwino kotheratu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero48 Nʼchifukwa chake, inu khalani angwiro monga Atate anu akumwamba ali wangwiro.” Onani mutuwo |