Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 5:27 - Buku Lopatulika

27 Munamva kuti kunanenedwa, Usachite chigololo;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

27 Munamva kuti kunanenedwa, Usachite chigololo;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

27 “Mudamva kuti anthu akale aja adaaŵalamula kuti, ‘Usachite chigololo.’

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

27 “Munamva kuti kunanenedwa kuti, ‘Usachite chigololo.’

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 5:27
10 Mawu Ofanana  

Usachite chigololo.


Wochita chigololo ndi mkazi alibe nzeru; wofuna kuononga moyo wakewake ndiye amatero.


Usagona naye mkazi wa mnansi wako, kudetsedwa naye limodzi.


Munthu akachita chigololo ndi mkazi wa mwini, popeza wachita chigololo ndi mkazi wa mnansi wake, awaphe ndithu, mwamuna ndi mkazi onse awiri.


Munamva kuti kunanenedwa kwa iwo akale, Usaphe; koma yense wakupha adzakhala wopalamula mlandu:


Ndiponso, munamva kuti kunanenedwa kwa iwo akale, Usalumbire konama, koma udzapereka kwa Ambuye zolumbira zako:


Munamva kuti kunanenedwa, Diso kulipa diso, ndi dzino kulipa dzino:


Munamva kuti kunanenedwa, Uzikondana ndi mnansi wako, ndi kumuda mdani wako:


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa