Mateyu 5:28 - Buku Lopatulika28 koma Ine ndinena kwa inu, kuti yense wakuyang'ana mkazi kumkhumba, pamenepo watha kuchita naye chigololo mumtima mwake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201428 koma Ine ndinena kwa inu, kuti yense wakuyang'ana mkazi kumkhumba, pamenepo watha kuchita naye chigololo mumtima mwake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa28 Chabwino, koma Ine ndikukuuzani kuti munthu aliyense woyang'ana mkazi ndi kumkhumba, wachita naye kale chigololo mumtima mwake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero28 Koma Ine ndikuwuzani kuti aliyense woyangʼana mkazi momusirira wachita naye kale chigololo mu mtima mwake. Onani mutuwo |