Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 5:21 - Buku Lopatulika

21 Munamva kuti kunanenedwa kwa iwo akale, Usaphe; koma yense wakupha adzakhala wopalamula mlandu:

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

21 Munamva kuti kunanenedwa kwa iwo akale, Usaphe; koma yense wakupha adzakhala wopalamula mlandu:

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

21 “Mudamva kuti anthu akale aja adaaŵalamula kuti, ‘Usaphe. Aliyense wopha mnzake adzayenera kuzengedwa ku bwalo lamilandu,’

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

21 “Munamva kuti kunanenedwa kwa anthu kale kuti, ‘Usaphe ndipo kuti aliyense amene apha munthu adzaweruzidwa.’

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 5:21
19 Mawu Ofanana  

Ndipo iye analankhula, nati, Kale adanena kuti, Zoonadi adzapempha uphungu ku Abele; ndipo potero mlandu udatha.


Naika oweruza m'dziko, m'mizinda yonse yamalinga ya mu Yuda, mzinda ndi mzinda;


Ndipo mizindayo ikukhalireni yakupulumuka wolipsa; kuti wakupha mnzake asafe, kufikira ataima pamaso pa msonkhano amweruze.


Munamva kuti kunanenedwa, Usachite chigololo;


Ndiponso, munamva kuti kunanenedwa kwa iwo akale, Usalumbire konama, koma udzapereka kwa Ambuye zolumbira zako:


Munamva kuti kunanenedwa, Diso kulipa diso, ndi dzino kulipa dzino:


Munamva kuti kunanenedwa, Uzikondana ndi mnansi wako, ndi kumuda mdani wako:


Mudziikire oweruza ndi akapitao m'midzi yanu yonse imene Yehova Mulungu wanu akupatsani, monga mwa mafuko anu; ndipo aweruze anthu ndi chiweruzo cholungama.


Yense wakudana ndi mbale wake ali wakupha munthu; ndipo mudziwa kuti wakupha munthu aliyense alibe moyo wosatha wakukhala mwa iye.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa