Mateyu 5:16 - Buku Lopatulika16 Chomwecho muwalitse inu kuunika kwanu pamaso pa anthu, kuti pakuona ntchito zanu zabwino, alemekeze Atate wanu wa Kumwamba. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Chomwecho muwalitse inu kuunika kwanu pamaso pa anthu, kuti pakuona ntchito zanu zabwino, alemekeze Atate wanu wa Kumwamba. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Chomwechonso inuyo muziwonetsa kuŵala kwanu pamaso pa anthu, kuti ataona ntchito zanu zabwino azilemekeza Atate anu akumwamba. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Momwemonso kuwunika kwanu kuwale pamaso pa anthu kuti aone ntchito zanu zabwino ndi kulemekeza Atate anu akumwamba. Onani mutuwo |