Mateyu 4:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo woyesayo anafika nanena kwa Iye, Ngati muli Mwana wa Mulungu, tauzani kuti miyala iyi isanduke mikate. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo woyesayo anafika nanena kwa Iye, Ngati muli Mwana wa Mulungu, tauzani kuti miyala iyi isanduke mikate. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Tsono Woyesa uja adadza namuuza kuti, “Ngati ndinu Mwana wa Mulungu, lamulani miyala ili apayi kuti isanduke chakudya.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Woyesayo anadza kwa Iye nati, “Ngati ndinu mwana wa Mulungu, sandutsani miyala iyi kuti ikhale buledi.” Onani mutuwo |