Mateyu 4:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo pamene Iye analibe kudya masiku makumi anai usana ndi usiku, pambuyo pake anamva njala. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo pamene Iye analibe kudya masiku makumi anai usana ndi usiku, pambuyo pake anamva njala. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Pa masiku makumi anai Yesu adasala zakudya usana ndi usiku, ndipo pambuyo pake adamva njala. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Ndipo atasala kudya masiku makumi anayi usana ndi usiku, anamva njala. Onani mutuwo |