Mateyu 4:12 - Buku Lopatulika12 Ndipo pamene Yesu anamva kuti anampereka Yohane, anamuka kulowa ku Galileya; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndipo pamene Yesu anamva kuti anampereka Yohane, anamuka kulowa ku Galileya; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Yesu atamva kuti Yohane adamponya m'ndende, adabwerera ku Galileya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Yesu atamva kuti Yohane anamutsekera mʼndende, anabwerera ku Galileya. Onani mutuwo |