Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 4:12 - Buku Lopatulika

12 Ndipo pamene Yesu anamva kuti anampereka Yohane, anamuka kulowa ku Galileya;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 Ndipo pamene Yesu anamva kuti anampereka Yohane, anamuka kulowa ku Galileya;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 Yesu atamva kuti Yohane adamponya m'ndende, adabwerera ku Galileya.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 Yesu atamva kuti Yohane anamutsekera mʼndende, anabwerera ku Galileya.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 4:12
13 Mawu Ofanana  

Koma Yohane, pakumva m'nyumba yandende ntchito za Khristu, anatumiza ophunzira ake mau,


Pakuti Herode adamgwira Yohane, nammanga, namuika m'nyumba yandende chifukwa cha Herodiasi, mkazi wa mbale wake Filipo.


Ndipo ataperekedwa Yohane, Yesu anadza ku Galileya, nalalikira Uthenga Wabwino wa Mulungu,


Pakuti Herode, mwini yekha, adatuma anthu namgwira Yohane, nammanga m'nyumba yandende, chifukwa cha Herodiasi, mkazi wa Filipo mbale wake; chifukwa adamkwatira iye.


Koma iwo anapunda kunena kuti, Amautsa anthuwo, naphunzitsa mu Yudeya yense, kuyambira ku Galileya ndi kufikira kuno komwe.


anaonjeza pa zonsezi ichinso, kuti anatsekera Yohane m'nyumba yandende.


Ndipo Yesu anabwera ndi mphamvu ya Mzimu ku Galileya; ndipo mbiri yake ya Iye inabuka ku dziko lonse loyandikira.


Ndipo Iye anatsika nadza ku Kapernao, ndiwo mzinda wa ku Galileya. Ndipo analikuwaphunzitsa iwo pa Sabata; ndipo anadabwa ndi chiphunzitso chake;


M'mawa mwake anafuna kutuluka kunka ku Galileya, napeza Filipo. Ndipo Yesu ananena naye, Tsata Ine.


Chiyambi ichi cha zizindikiro zake Yesu anachita mu Kana wa mu Galileya naonetsera ulemerero wake; ndipo ophunzira ake anakhulupirira Iye.


Pakuti Yohane sanaikidwe m'ndende.


Koma atapita masiku awiriwo anachoka komweko kunka ku Galileya.


Ichi ndi chizindikiro chachiwiri Yesu anachita, atachokera ku Yudeya, ndi kulowa mu Galileya.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa