Mateyu 4:13 - Buku Lopatulika13 ndipo anachoka ku Nazarete nadza nakhalitsa Iye mu Kapernao wa pambali pa nyanja, m'malire a Zebuloni ndi Nafutali: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 ndipo anachoka ku Nazarete nadza nakhalitsa Iye m'Kapernao wa pambali pa nyanja, m'malire a Zebuloni ndi Nafutali: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Adachokako ku Nazarete, nakakhala ku Kapernao, mzinda wina wa m'mbali mwa nyanja ku dera la Zebuloni ndi Nafutali. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Ndipo atachoka ku Nazareti anapita ku Kaperenawo ndi kukhala mʼmbali mwa nyanja, mʼdera la Zebuloni ndi Nafutali; Onani mutuwo |