Mateyu 28:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo onani, Yesu anakomana nao, nanena, Tikuoneni. Ndipo iwo anadza, namgwira Iye mapazi ake, namgwadira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo onani, Yesu anakomana nao, nanena, Tikuoneni. Ndipo iwo anadza, namgwira Iye mapazi ake, namgwadira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Mwadzidzidzi Yesu adakumana nawo nati, “Monitu azimai!” Iwo adadza pafupi, nkugwira mapazi ake, nampembedza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Mwadzidzidzi Yesu anakumana nawo nati, “Moni.” Iwo anabwera kwa Iye, nagwira mapazi ake namulambira. Onani mutuwo |