Mateyu 28:5 - Buku Lopatulika5 Koma mngelo anayankha, nati kwa akaziwo, Musaope inu; pakuti ndidziwa inu mulikufuna Yesu, amene anapachikidwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Koma mngelo anayankha, nati kwa akaziwo, Musaope inu; pakuti ndidziwa inu mulikufuna Yesu, amene anapachikidwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Koma mngeloyo adalankhula ndi azimai aja naŵauza kuti, “Inu musaope ai. Ndikudziŵa kuti mukufuna Yesu, uja adaampachika pa mtandayu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Mngelo anati kwa amayiwo, “Musachite mantha popeza ndikudziwa kuti mukufuna Yesu amene anapachikidwa. Onani mutuwo |