Mateyu 28:4 - Buku Lopatulika4 ndipo ndi kuopsa kwake alondawo ananthunthumira, nakhala ngati anthu akufa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 ndipo ndi kuopsa kwake alondawo ananthunthumira, nakhala ngati anthu akufa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Pamenepo alonda aja adachita mantha nayamba kunjenjemera, nkungoti gwa ngati anthu akufa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Alondawo anachita naye mantha kwambiri kotero kuti ananjenjemera ndi kuwuma ngati akufa. Onani mutuwo |