Mateyu 28:16 - Buku Lopatulika16 Koma ophunzira khumi ndi mmodziwo anamuka ku Galileya, kuphiri kumene Yesu anawapangira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Koma ophunzira khumi ndi mmodziwo anamuka ku Galileya, kuphiri kumene Yesu anawapangira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Ophunzira khumi ndi mmodzi aja adapita ku Galileya kuphiri kumene Yesu adaapangana nawo kuti akakumane. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Ndipo ophunzira khumi ndi mmodzi aja anapita ku Galileya, ku phiri limene Yesu anawawuza kuti apite. Onani mutuwo |