Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Mateyu 28:17 - Buku Lopatulika

17 Ndipo pamene anamuona Iye, anamlambira; koma ena anakayika.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 Ndipo pamene anamuona Iye, anamlambira; koma ena anakayika.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 Pamene adamuwona, adampembedza, koma ena ankakayika.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 Atamuona Iye, anamulambira; koma ena anakayika.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 28:17
10 Mawu Ofanana  

Mpsompsoneni Mwanayo, kuti angakwiye, ndipo mungatayike m'njira ukayaka pang'ono pokha mkwiyo wake. Odala onse akumkhulupirira Iye.


potero mfumuyo adzakhumba kukoma kwako, pakuti ndiye mbuye wako; ndipo iwe umgwadire iye.


Indetu ndinena kwa inu, kuti alipo ena a iwo aima pano sadzalawa ndithu imfa, kufikira adzaona Mwana wa Munthu atadza mu ufumu wake.


Ndipo onani, Yesu anakomana nao, nanena, Tikuoneni. Ndipo iwo anadza, namgwira Iye mapazi ake, namgwadira.


Ndipo iwowo, pamene anamva kuti ali moyo, ndi kuti adapenyeka kwa iye, sanamvere.


Ndipo iwowa anachoka nawauza otsala; koma iwo omwe sanawavomereze.


Ndipo chitatha icho anaonekera kwa khumi ndi mmodzi iwo okha, alikuseama pachakudya; ndipo anawadzudzula chifukwa cha kusavomereza kwao ndi kuuma mtima, popeza sanavomereze iwo amene adamuona, atauka Iye.


kuti onse akalemekeze Mwana, monga alemekeza Atate. Wosalemekeza Mwana salemekeza Atate amene anamtuma Iye.


kwa iwonso anadzionetsera yekha wamoyo ndi zitsimikizo zambiri, zitatha zowawa zake, naonekera kwa iwo masiku makumi anai, ndi kunena zinthu za Ufumu wa Mulungu;


pomwepo anaoneka pa nthawi imodzi kwa abale oposa mazana asanu, amene ochuluka a iwo akhala kufikira tsopano, koma ena agona;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa