Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 28:13 - Buku Lopatulika

13 nati, Kazinenani, kuti ophunzira ake anadza usiku, namuba Uja m'mene ife tinali m'tulo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 nati, Kazinenani, kuti ophunzira ake anadza usiku, namuba Uja m'mene ife tinali m'tulo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 naŵauza kuti, “Muziti, ‘Ophunzira ake anabwera usiku nkuba mtembo wake ife tili m'tulo.’

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 nawawuza kuti, “Muzinena kuti, ‘Ophunzira ake anabwera usiku ndipo amuba ife tili mtulo.’

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 28:13
3 Mawu Ofanana  

Yesu anati kwa iye, Mwatero, koma ndinenanso kwa inu, Kuyambira tsopano mudzaona Mwana wa Munthu ali kukhala kudzanja lamanja la mphamvu, ndi kufika pa mitambo ya kumwamba.


Ndipo pamene anasonkhana pamodzi ndi akulu, anakhala upo, napatsa asilikaliwo ndalama zambiri,


Ndipo ngati ichi chidzamveka kwa kazembe, ife tidzamgwetsa mtima, ndipo tidzakukhalitsani opanda nkhawa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa