Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Mateyu 28:14 - Buku Lopatulika

14 Ndipo ngati ichi chidzamveka kwa kazembe, ife tidzamgwetsa mtima, ndipo tidzakukhalitsani opanda nkhawa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

14 Ndipo ngati ichi chidzamveka kwa kazembe, ife tidzamgwetsa mtima, ndipo tidzakukhalitsani opanda nkhawa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

14 Choncho bwanamkubwa akamva zimenezi, ife tidzamkhazika mtima pansi, ndipo sipadzakhala kanthu kokuvutani.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

14 Ngati nkhani iyi imupeze bwanamkubwa, ife tidzamukhazika mtima pansi ndipo simudzakhala mʼmavuto.”

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 28:14
3 Mawu Ofanana  

ndipo anammanga Iye, namuka naye, nampereka Iye kwa Pilato kazembeyo.


nati, Kazinenani, kuti ophunzira ake anadza usiku, namuba Uja m'mene ife tinali m'tulo.


Ndipo pamene Herode adamfunafuna, wosampeza, anafunsitsa odikira nalamulira aphedwe. Ndipo anatsika ku Yudeya kunka ku Kesareya, nakhalabe kumeneko.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa