Mateyu 27:61 - Buku Lopatulika61 Ndipo Maria wa Magadala anali pamenepo, ndi Maria winayo, anakhala pansi popenyana ndi mandawo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201461 Ndipo Maria wa Magadala anali pamenepo, ndi Maria winayo, anakhala pansi popenyana ndi mandawo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa61 Maria wa ku Magadala ndi Maria wina uja anali pomwepo atakhala pansi kuyang'anana ndi mandawo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero61 Mariya wa Magadala ndi Mariya wina anakhala pansi moyangʼanizana ndi mandawo. Onani mutuwo |