Mateyu 27:56 - Buku Lopatulika56 mwa iwo amene munali Maria wa Magadala, ndi Maria amake wa Yakobo, ndi wa Yosefe, ndi amake wa ana a Zebedeo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201456 mwa iwo amene munali Maria wa Magadala, ndi Maria amake wa Yakobo, ndi wa Yosefe, ndi amake wa ana a Zebedeo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa56 Pakati pao panali Maria wa ku Magadala, Maria mai wa Yakobe ndi Yosefe, ndiponso mai wa ana a Zebedeo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero56 Pakati pawo panali Mariya wa ku Magadala, Mariya amayi ake Yakobo ndi Yosefe ndi amayi a ana a Zebedayo. Onani mutuwo |