Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 27:49 - Buku Lopatulika

49 Koma ena anati, Taleka, tione ngati Eliya adzafika kudzampulumutsa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

49 Koma ena anati, Taleka, tione ngati Eliya adzafika kudzampulumutsa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

49 Koma ena adati, “Taima, tiwone ngati Eliya abweredi kudzampulumutsa.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

49 Koma ena onse anati, “Mulekeni tiyeni tione ngati Eliyayo abwere kudzamupulutsa.”

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 27:49
4 Mawu Ofanana  

Ndipo Eliya wa ku Tisibe wokhala ku Giliyadi ananena ndi Ahabu, nati, Pali Yehova Mulungu wa Israele, amene ndimakhala pamaso pake, ngati adzagwa mame kapena mvula zaka izi, koma ntanena ine ndipo.


ndi kuti, Wamsiya Mulungu. Mlondoleni, mgwireni; popeza palibe wompulumutsa.


Ndipo pomwepa mmodzi wa iwo anathamanga, natenga chinkhupule, nachidzaza ndi vinyo wosasa, nachiika pabango, namwetsa Iye.


Ndipo Yesu, pamene anafuula ndi mau aakulu, anapereka mzimu wake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa