Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 27:48 - Buku Lopatulika

48 Ndipo pomwepa mmodzi wa iwo anathamanga, natenga chinkhupule, nachidzaza ndi vinyo wosasa, nachiika pabango, namwetsa Iye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

48 Ndipo pomwepa mmodzi wa iwo anathamanga, natenga chinkhupule, nachidzaza ndi vinyo wosasa, nachiika pabango, namwetsa Iye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

48 Motero wina adathamanga nakatenga chinkhupule. Adachiviika m'vinyo wosasa, nkuchitsomeka ku bango nampatsira, kuti amwe.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

48 Mmodzi wa iwo anathamanga natenga chinkhupule. Anachidzaza ndi vinyo wosasa, nachizika ku mtengo namupatsa Yesu kuti amwe.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 27:48
7 Mawu Ofanana  

Ndipo anandipatsa ndulu ikhale chakudya changa; nandimwetsa vinyo wosasa pomva ludzu ine.


anamwetsa Iye vinyo wosakaniza ndi ndulu; ndipo Iye, m'mene analawa, sanafune kumwa.


Ndipo ena a iwo akuimirira komweko, pamene anamva, ananena, Uyo aitana Eliya.


Koma ena anati, Taleka, tione ngati Eliya adzafika kudzampulumutsa.


Ndipo anathamanga wina, nadzaza chinkhupule ndi vinyo wosasa, nachiika pabango, namwetsa Iye, nanena, Lekani; tione ngati Eliya adza kudzamtsitsa.


Ndipo asilikalinso anamnyoza, nadza kwa Iye, nampatsa vinyo wosasa,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa