Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 27:47 - Buku Lopatulika

47 Ndipo ena a iwo akuimirira komweko, pamene anamva, ananena, Uyo aitana Eliya.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

47 Ndipo ena a iwo akuimirira komweko, pamene anamva, ananena, Uyo aitana Eliya.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

47 Atamva mauwo, ena amene adaaimirira pamenepo adati, “Munthuyu akuitana Eliya.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

47 Ena a oyimirira pamalopo atamva izi anati, “Akuyitana Eliya.”

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 27:47
5 Mawu Ofanana  

Taonani, ndidzakutumizirani Eliya mneneri lisanadze tsiku lalikulu ndi loopsa la Yehova.


Ndipo ngati mufuna kulandira, uyu ndiye Eliya amene amati akudza.


Ndipo poyandikira ora lachisanu ndi chinai, Yesu anafuula ndi mau aakulu, kunena, Eli, Eli, lama sabakitani? ndiko kunena kuti, Mulungu wanga, Mulungu wanga, mwandisiyiranji Ine?


Ndipo pomwepa mmodzi wa iwo anathamanga, natenga chinkhupule, nachidzaza ndi vinyo wosasa, nachiika pabango, namwetsa Iye.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa