Mateyu 27:4 - Buku Lopatulika4 nanena, Ndinachita koipa ine, pakupereka mwazi wosalakwa. Koma iwo anati, Tili nacho chiyani ife? Udzionere wekha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 nanena, Ndinachita koipa ine, pakupereka mwazi wosalakwa. Koma iwo anati, Tili nacho chiyani ife? Udzionere wekha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Adati, “Ndidachimwa pakupereka munthu wosalakwa kuti aphedwe.” Koma iwo adati, “Ife tilibe nazo kanthu. Izo nzako.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Iye anati, “Ndachimwa pakuti ndapereka munthu wosalakwa.” Iwo anayankha nati, “Ife tilibe nazo kanthu izo ndi zako.” Onani mutuwo |